nya-x-nyanja_rev_text_reg/02/10.txt

1 line
337 B
Plaintext

\v 10 Musayope zoipa zamene muzapitamo. Onani! satana azaponya benangu ba inu mu ndende kuti mukayesedwe, ndipo muzabvutika kwa masiku 10. Nkhalani okhulupirika mpaka kufa, elo nizakupasani kolona ya moyo. \v 11 Lekani amene ali na matu ya kumva amvere zamene mzimu ukamba kwa mipingo. Iye amene apambana sazaonongeka na imfa ya chiwiri.