nya-x-nyanja_rev_text_reg/01/07.txt

1 line
261 B
Plaintext

\v 7 Onani, azabwera mu makumbi; ndipo diso lililose lizamuona, kuikapo naonse bamene banamulasa. Ziko lonse lizalira chifukwa cha yeve. Inde, Amen. \v 8 "Ndine oyamba na osiliza," akamba ambuye Mulungu, "amene analiko, aliko, elo azankhalako, wa mpamvu zonse."