Thu Jan 02 2020 18:42:41 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
Bshop2 2020-01-02 18:42:42 +02:00
parent dc4e19c2cd
commit 806e40d904
7 changed files with 12 additions and 6 deletions

View File

@ -1 +1 @@
\v 4 \v 5 \v 6 Yohane, ku mipingo isanu na iwiri ya ku Asiya: Cisomo ni mtendere kucokera kwa iye amene analiko, aliko ndipo azankhalako, ni kwa mizimu isanu ni iwiri yamene yankhala pa mpando wa cimfumu, na kwa Yesu Khristu, amene ni mboni yokhulupirika, mwana oyamba kucoka pa akufa, ni olamulira mamfumu a dziko lapansi. Kwa iye wamene atikonda ndipo anatiombola ku machimo athu ni magazi yace- watipanga kunkhala umfumu, ansembe a Mulungu wake Atate- kwa iye kunkhale ulemelero ni mphamvu kwa nthawi zonse. Amen.
\v 4 Yohane, ku mipingo isanu na iwiri ya ku Asiya: Cisomo ni mtendere kucokera kwa iye amene analiko, aliko ndipo azankhalako, ni kwa mizimu isanu ni iwiri yamene yankhala pa mpando wa cimfumu, \v 5 na kwa Yesu Khristu, amene ni mboni yokhulupirika, mwana oyamba kucoka pa akufa, ni olamulira mamfumu a dziko lapansi. Kwa iye wamene atikonda ndipo anatiombola ku machimo athu ni magazi yace- \v 6 watipanga kunkhala umfumu, ansembe a Mulungu wake Atate- kwa iye kunkhale ulemelero ni mphamvu kwa nthawi zonse. Amen.

View File

@ -1 +1 @@
\v 7 \v 8 Onani, azabwera mu makumbi; ndipo diso lililose lizamuona, kuikapo naonse bamene banamulasa. Ziko lonse lizalira chifukwa cha yeve. Inde, Amen. "Ndine oyamba na osiliza," akamba ambuye Mulungu, "amene analiko, aliko, elo azankhalako, wa mpamvu zonse."
\v 7 Onani, azabwera mu makumbi; ndipo diso lililose lizamuona, kuikapo naonse bamene banamulasa. Ziko lonse lizalira chifukwa cha yeve. Inde, Amen. \v 8 "Ndine oyamba na osiliza," akamba ambuye Mulungu, "amene analiko, aliko, elo azankhalako, wa mpamvu zonse."

View File

@ -1 +1 @@
\v 9 \v 10 \v 11 Ine, Yohane-m'bale wanu amene agabana na inu zobvuta na kupilira zamene zipezeka mwa Yesu- ninali pa malo ozungulilidwa na manzi ya Patmos kamba ka mau ya Mulungu na umboni wa Yesu. Ninali mu mzimu wa siku la ambuye. Ninamvera kumbuyo kwanga mau okuwa omveka monga lipenga. Yanakamba ati, "lemba zamene uona mu buku, elo uzitume ku mipingo isanu na iwiri- ku Efeso, ku Smyrna, ku Pergamum, ku Thyatira, ku Sardis, ku Philadelphia na ku Laodicea."
\v 9 Ine, Yohane-m'bale wanu amene agabana na inu zobvuta na kupilira zamene zipezeka mwa Yesu- ninali pa malo ozungulilidwa na manzi ya Patmos kamba ka mau ya Mulungu na umboni wa Yesu. \v 10 Ninali mu mzimu wa siku la ambuye. Ninamvera kumbuyo kwanga mau okuwa omveka monga lipenga. \v 11 Yanakamba ati, "lemba zamene uona mu buku, elo uzitume ku mipingo isanu na iwiri- ku Efeso, ku Smyrna, ku Pergamum, ku Thyatira, ku Sardis, ku Philadelphia na ku Laodicea."

View File

@ -1 +1 @@
\v 12 \v 13 Ninapindamuka kuti nione ni mau ya bandani yamene yenze kunikambisa, pamene ninapindamuka ninaona pofaka nyale pagolide pali 7. Pakati pa nyale panali wina wamene anaoneka monga mwana wa munthu, anabvala mukanjo utali maningi wamene unafika ku mendo yake na sashi ya golide kuzungulira chifuba chake.
\v 12 Ninapindamuka kuti nione ni mau ya bandani yamene yenze kunikambisa, pamene ninapindamuka ninaona pofaka nyale pagolide pali 7. \v 13 Pakati pa nyale panali wina wamene anaoneka monga mwana wa munthu, anabvala mukanjo utali maningi wamene unafika ku mendo yake na sashi ya golide kuzungulira chifuba chake.

View File

@ -1 +1 @@
\v 14 \v 15 \v 16 Mutu wake na sisi zinali zoyera monga thonje- zoyera monga matalala, elo menso yake yenze yosweta monga muliro. Mapazi yake yenze yobeka monga ni bronze, bronze yakuti baifaka pa muliro, elo mau yake yenzomveka monga ni manzi yambiri. Enze anagwira nyenyezi 7 kumanja yake, na mpeni wamene uchekera mbali zonse unali kuchoka mukamwa mwake. Pamenso pake penzowala monga ni zuba.
\v 14 Mutu wake na sisi zinali zoyera monga thonje- zoyera monga matalala, elo menso yake yenze yosweta monga muliro. \v 15 Mapazi yake yenze yobeka monga ni bronze, bronze yakuti baifaka pa muliro, elo mau yake yenzomveka monga ni manzi yambiri. \v 16 Enze anagwira nyenyezi 7 kumanja yake, na mpeni wamene uchekera mbali zonse unali kuchoka mukamwa mwake. Pamenso pake penzowala monga ni zuba.

View File

@ -1 +1 @@
\v 17 \v 18 Pamene ninamuona, ninagwa pansi pa mendo yake monga munthu wakufa. Anafaka zanja yake pali ine ndipo anakamba ati, "usayope. ndine oyamba na osiliza, na wamene ankhala na moyo. Ninali wakufa, koma onani, ninkhala wa muyayaya! elo nili na mfungulo ya imfa na hade.
\v 17 Pamene ninamuona, ninagwa pansi pa mendo yake monga munthu wakufa. Anafaka zanja yake pali ine ndipo anakamba ati, "usayope. ndine oyamba na osiliza, \v 18 na wamene ankhala na moyo. Ninali wakufa, koma onani, ninkhala wa muyayaya! elo nili na mfungulo ya imfa na hade.

View File

@ -44,6 +44,12 @@
"finished_chunks": [
"front-title",
"01-title",
"01-04",
"01-07",
"01-09",
"01-12",
"01-14",
"01-17",
"10-01",
"10-03",
"10-05",