nya-x-nyanja_rev_text_reg/09/03.txt

1 line
245 B
Plaintext
Raw Normal View History

\v 3 Kuchoka mu utsi dzombe unabwera pa dziko la pansi, ndipo inapasidwa mphamvu monga za kaliza pa dziko la pansi. \v 4 Yanauziwa kuti yasaononge mitengo kapena udzu pa dziko, koma chabe anthu amene alibe chizindikiro cha Mulungu pa mphumi pao.