|
\v 41 Ndipo Yesu anakhala pansi pafupi ndi thumba yopelekelamo zambale; analikuona anthu ali kupeleka ndalama mthumba. Anthu ambiri wolemela analikupeleka ndalama zambiri. \v 42 Koma wosauka wamasiye anabwela ndi tungwinjiri tuwili, tolingana na peni. |