nya-x-nyanja_mrk_text_reg/12/41.txt

1 line
251 B
Plaintext

\v 41 Ndipo Yesu anakhala pansi pafupi ndi thumba yopelekelamo zambale; analikuona anthu ali kupeleka ndalama mthumba. Anthu ambiri wolemela analikupeleka ndalama zambiri. \v 42 Koma wosauka wamasiye anabwela ndi tungwinjiri tuwili, tolingana na peni.