nya-x-nyanja_mrk_text_reg/12/24.txt

1 line
218 B
Plaintext

\v 24 Yesu anati, "Ici sindiye cifukwa cake mulakwisa, Cifukwa simuziwa malembo kapena mpamvu ya Mulungu? \v 25 Pamene azauka kwa kufa, Sikuzakhala kukwatira kapena kukwatiliwa, koma azankhala ngati Angelo a kumwamba.