nya-x-nyanja_mrk_text_reg/12/16.txt

1 line
215 B
Plaintext

\v 16 Anabwelesa imozi kwa Yesu. Anati kwa iye, "Kodi pali mutu ndi malemba andani?" Iwo nati, "Kaisayi" \v 17 Yesu anati, Pelekani kwa Kaisayi zinthu za Kaisayi ndi kwa Mulungu zinthu za Mulungu." Anadabwa ndi iye.