nya-x-nyanja_mrk_text_reg/10/35.txt

1 line
305 B
Plaintext

\v 35 Yakobo ndi Yohane ana a Zebediya anabwela kwa iye anati, ''Mphuzisi, tifuna inu kuti m'tichitire virivotse vamene tizakupemphani." \v 36 Anakamba kwa iwo anati, Mufuna kuti ine nikucitireni ciani? \v 37 ''Tiloleni kuti tikakhale nayinu muulemelelo wanu, umonzi kuzanjalamanjai ndi wina kulamanzele."