nya-x-nyanja_mrk_text_reg/10/23.txt

1 line
350 B
Plaintext

\v 23 Yesu anayangana-yangana ndikuuza wophunzila ake nati, "Onani kukosa kwa iwo wolemela kungena ufumu wa Mulungu." \v 24 Wophunzila ake anadabwa pa mau aya. Koma Yesu analakulanso kwa iwo nati, "Ana, Nikovuta kungena ufumu wa Mulungu! \v 25 Ciliko capafupi ngamila kungena pamulomo wa nyeleti, kupambana munthu wolemela kungena ufumu wa Mulungu,"