nya-x-nyanja_mrk_text_reg/06/53.txt

1 line
268 B
Plaintext

\v 53 Pamene anafika kusidya ina yacimana, anafika kumalo wocedwa Genesareti ndipo anaimisa boti. \v 54 Pamene anaseluka mu boti, anamuzindikira iye. \v 55 Ndipo anathamanga m'muzinda ndikuyamba kubwelesa wodwala kwa iye pamamphasa, kwamene anavelela kuti alikupitira.