nya-x-nyanja_mrk_text_reg/06/07.txt

1 line
301 B
Plaintext

\v 7 Ndipo anaitana aja twelufu (12) ndikuwatuma kuti apite awili - awili, ndipo anawapasa ulamuliro pamizimu yonyansa, \v 8 anawalamulira kuti asanyamule ciliconse paulendo, koma cabe ndodo: asanyamule buledi, kapena thumba, kapena ndalama mucikwama, \v 9 koma avale nkwabilo asavwale minjilo iwili.