nya-x-nyanja_mrk_text_reg/06/01.txt

1 line
497 B
Plaintext

\c 6 \v 1 Ndipo ancokako kuja ndi kupita kumuzida wake, ndipo wophunzira anamusata iye. \v 2 Pamene sabata inafika anali kuphunzitsa musunagoge. Anthu ambiri anamva ndipo anadabwisika. Anati, "Anacotsa kuti ziphunziso zotele?" "Kodi nzelu izi zamene zinapasidwa kwa iye nizabwanji?" "Nanga izi zodabwitsa zamene iye ali kucita?" \v 3 "Kodi uyu siuja mpala mathabwa mwana wa Maliya and mkwawo wa Yakobo na Joses na Yudas na Simoni? Nipo alongo ake sali naife pano?" Ndipo anakumudwisiwa ndi Yesu.