nya-x-nyanja_mrk_text_reg/05/36.txt

1 line
337 B
Plaintext

\v 36 Koma pamene Yesu anamvako zimene analikulankhula, iye anati kumtsogoleli wa sunagogi, "Usacite mantha. Kuluphilira cabe." \v 37 Sanavomeze kuti wina ayende naye, koma Petulo, Yakobo ndi Yohana, ndimbale wa Yakobo. \v 38 Anafika kunyumba kwa uja mtsogoleli ndi anaona anthu ambiri alikumpanga congo; analikulira ndikupunda kwambiri.