nya-x-nyanja_jos_text_reg/09/22.txt

1 line
281 B
Plaintext

\v 22 Yoswa anabaitana na kukamba kuti, '' cifukwa nicani ananinama pamene unakamba, tili kutali naimwe,' pamene ukhala pakati kaise? \v 23 Manje, cifukwa caici, ndiwe otembeleleka nabena baimwe muzayamba kukhala akapolo, naja wodula maplanga na botapa manzi ya nyuma ya mulungu.''