nya-x-nyanja_jos_text_reg/09/06.txt

1 line
398 B
Plaintext

\v 6 Ndipo banayenda kuli Yoswa mucipono ca Giligala nakukamba naye naba muna ba mu Israyeli,'' tacokela kuziko yakutali, Apa manje panga cipangano naise.'' \v 7 Bamuna bamo Israyeli banakamba kuli ba Hivites, '' kapena munkhala pafupi naise. Tingapange bwanji cipangano naimwe?'' \v 8 Banamba kuli Yoswa kuti,'' Ise ndise batumiki bano.'' Yoswa anakamba na beve, '' Ndiwe ndini? munacokele kuti?''