nya-x-nyanja_jos_text_reg/14/12.txt

1 line
250 B
Plaintext

\v 12 Manje apa nipaseni iyi phili yaziko, yamene Yehova ananilonjeza pasiku ija. Popeza munamvela siku ija kuti ba Anakim banali kuja namizinda zikulu za malinga. cingakhale kuti Yehova azakhala naine nakuti nizaba cosamo, monga Yehova anakambila.''