nya-x-nyanja_jos_text_reg/09/09.txt

1 line
331 B
Plaintext

\v 9 banakamba kuli iye,'' Batumitiki bako babwela kuno kucokela kumalo yakutali, cifukwa ca zina ya Yehova mulungu wanu. Tamvela pali yeve na pali vonse anacita mu Eigipito - \v 10 navonse anacita kuli mafumu yabili yako Amoni kumbali ina ya Yolodani - kuli sihon mfumu ya Heshbon, na ku og mfumu ya Bashan amene enze pa Ashtaota.