nya-x-nyanja_job_text_reg/28/26.txt

1 line
229 B
Plaintext

\v 26 Amalamulila mvula na kupanga njila ya kaleza. \v 27 Anaona nzelu nakuzilalikila; anazimapanga, zoona, nakuziyesa. \v 28 Kubantu anakamba kuti, 'yanganani, kuyopa kwa Ambuye-iyo ndiye nzelu; kucoka ku coipa ndiye kumvesesa."