nya-x-nyanja_job_text_reg/36/01.txt

1 line
273 B
Plaintext

\c 36 \v 1 \v 2 \v 3 Elihu anapitiliza kunena kuti, "Ndiloleni ndilankhule kwa kanthawi kochepa, ndikuwonetsani zinthu zina chifukwa ndili ndi zambiri zoti ndinene poteteza Mulungu. Ndidzazindikira kuchokera kutali, ndidzazindikira kuti chilungamo ndi cha kwa Mlengi wanga.