nya-x-nyanja_job_text_reg/19/15.txt

1 line
218 B
Plaintext

\v 15 Iwo amene adakhalapo monga alendo m'nyumba mwanga ndi adzakazi anga amandiona ngati mlendo; Ndine mlendo pamaso pawo. \v 16 Ndinaitana wantchito wanga, koma sandiyankha, Ngakhale ndinkamupempha ndi pakamwa panga.