nya-x-nyanja_job_text_reg/19/07.txt

1 line
247 B
Plaintext

\v 7 Onani, ndifuwula, "Chiwawa!" koma sindimayankhidwa. Ndifuulira thandizo, koma palibe chilungamo. \v 8 Wakhoma njira yanga kuti ndisadutse, Ndipo wayika mdima panjira yanga. \v 9 Wandilanda ulemerero wanga, ndipo wandilanda chisoti chachifumu.