\v 7 Onani, ndifuwula, "Chiwawa!" koma sindimayankhidwa. Ndifuulira thandizo, koma palibe chilungamo. \v 8 Wakhoma njira yanga kuti ndisadutse, Ndipo wayika mdima panjira yanga. \v 9 Wandilanda ulemerero wanga, ndipo wandilanda chisoti chachifumu.