1 line
283 B
Plaintext
1 line
283 B
Plaintext
\v 21 Pakuti maso a Mulungu amayang'ana njira za munthu; amapenya mayendedwe ake onse. \v 22 Palibe mdima, kapena mdima wandiweyani kumene ochita zosalungama angabisalire. \v 23 Pakuti Mulungu safunikiranso kusanthula munthu; palibe chifukwa choti munthu aliyense apite kukamuweruza. |