1 line
332 B
Plaintext
1 line
332 B
Plaintext
\v 10 Chifukwa chake, ndimvereni, inu anzeru: kuti kutari ndi Mulungu kuchita zoyipa; kukhale kutali ndi Wamphamvuyonse kuchita tchimo. \v 11 Pakuti amabwezera ntchito ya munthu; amachititsa munthu aliyense kubwezera mphotho ya njira zake. \v 12 Ndithudi, Mulungu sachita choipa chilichonse, ndipo Wamphamvuyonse sapotoza chiweruzo. |