|
\v 12 Si Mulungu ankala kutali maningi kumwamba? yangana kutalimpa kwa nyenyezi, patali pamene zilili! \v 13 Mukuti, 'Mulungu aziba cani? angaweluze mu mudima ukulu? \v 14 Makumbi yotikama yamuvinikila, mwakuti samationa; amayenda pa cikumbi cakumwamba.' |