1 line
305 B
Plaintext
1 line
305 B
Plaintext
\v 25 Koma ine, ndidziwa kuti Muomboli wanga ali ndi moyo, ndi kuti potsiriza adzaimirira padziko lapansi; \v 26 khungu langa, ndiko kuti, thupi ili, litawonongeka, pamenepo m'thupi langa ndidzawona Mulungu. \v 27 Ndidzamuwona ndi maso angawa — ine, osati munthu wina. Mtima wanga walefuka mkati mwanga. |