nya-x-nyanja_isa_text_reg/50/02.txt

1 line
356 B
Plaintext

\v 2 Chifukwa nichanoi nibwele uko popeza kulibe alionse? nitana kulibe ayanka? bushe kwanja yanga iyifupi kuti ninga kulipilile?bushe mulibe mpavwu muli ine kukupulumusa? Ona, muzulu kwanga nimayumika mimana, nimapanga mimana monga chipululu; nsomba zao zimafa mulandu wakusoba manzi nakuwola. \v 3 Nimavulika mu mwamba nimudima; navuikila na chinyula.''