nya-x-nyanja_isa_text_reg/22/10.txt

1 line
229 B
Plaintext

\v 10 Munawerenga nyumba za mu Yerusalemu, ndipo munagumula nyumba zanu kuti mulimbitse linga. \v 11 Munapanga dziwe pakati pa makoma awiri a madzi a dziwe lakale. Koma iwe sunaganizire wopanga mzindawo, amene adaupanga kalekale.