nya-x-nyanja_isa_text_reg/19/18.txt

1 line
328 B
Plaintext

\v 18 Pasiku ya pazankala mizinda ili d muzika ya Igipito bamene baza kamba chitundu chaku kanani, naku lumbila kuli Yehova wa kamumu umozi mwa mizinda iyi uazitanidwa kuti muizinda. ***Mumalo mwakuti muzinda wa zuba, atantauza muzinda waku Heliopolis, Matebensidwe akudala naya manje,atembenuza kuti muzinda wa chikonongeka.***