Sat Oct 02 2021 14:52:02 GMT+0200 (Central Africa Time)
This commit is contained in:
parent
7f6b1205f4
commit
cf94e24c79
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 12 Atero Yehova, Ndidzafalitsa ngati iye ngati mtsinje, ndi chuma cha amitundu ngati mtsinje wosefukira; mudzayamwa pambali pake, mudzanyamulidwa m'manja mwake, ndipo mudzakomedwa pa mawondo ake. \v 13 Monga mayi amatonthoza mwana wake, momwemo ndidzakutonthozani inu, mutonthozedwe mu Yerusalemu.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 14 Mudzaona izi, ndipo mtima wanu udzasangalala, ndipo mafupa anu adzaphuka ngati msipu. Dzanja la Yehova lidzadziwika kwa atumiki ake, koma adzasonyeza mkwiyo wake pa adani ake.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 15 Pakuti taonani, Yehova adza ndi moto, ndipo magareta ake akudza ngati namondwe kuti abweretse mkwiyo wake ndi kudzudzula ndi malawi amoto. \v 16 Pakuti Yehova adzaweruza anthu ndi moto, ndi lupanga lake. Anthu amene adzaphedwe ndi Yehova adzakhala ambiri.
|
|
@ -757,6 +757,8 @@
|
|||
"66-06",
|
||||
"66-07",
|
||||
"66-09",
|
||||
"66-10"
|
||||
"66-10",
|
||||
"66-12",
|
||||
"66-14"
|
||||
]
|
||||
}
|
Loading…
Reference in New Issue