Fri Oct 01 2021 16:37:30 GMT+0200 (Central Africa Time)
This commit is contained in:
parent
4edcea6aae
commit
60752abeb8
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 20 Tsiku lomwelo ndidzayitana mtumiki wanga Eliyakimu mwana wa Hilikiya. \v 21 Ndidzamuveka iye malaya ako, ndi kumveka lamba wako; ndipo ndidzampatsa ulamuliro wako m'dzanja lake. Iye adzakhala atate wa okhala m'Yerusalemu ndi nyumba ya Yuda. \v 22 Ndidzaika kiyi wa nyumba ya Davide paphewa pake. adzatsegula, ndipo palibe amene adzatseke; adzatseka, ndipo palibe amene adzatsegule.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 23 Ndidzamukhomerera, ngati msomali pamalo okhazikika, ndipo iye adzakhala mpando wa ulemu m'nyumba ya atate wake. \v 24 Adzapachika pa iye ulemu wonse wam'nyumba ya abambo ake, ana ndi zidzukulu, chidebe chilichonse chaching'ono kuyambira pamakapu mpaka mitsuko yonse.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 25 Tsiku lomwelo, atero Yehova wa makamu, msomali wokhomedwa wolimba udzagwedezeka, nudzagwetsedwa, ndi kugwa;
|
|
@ -261,6 +261,8 @@
|
|||
"22-12",
|
||||
"22-15",
|
||||
"22-17",
|
||||
"22-20",
|
||||
"22-23",
|
||||
"24-title",
|
||||
"24-01",
|
||||
"24-03",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue