Fri Oct 01 2021 17:14:31 GMT+0200 (Central Africa Time)
This commit is contained in:
parent
20b01113b2
commit
0f2eafadcd
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 10 Oomboledwa a Yehova adzabwera nadzafika ku Ziyoni akuyimba, ndi chimwemwe chosatha chidzakhala pa mitu yawo; kukondwa ndi chimwemwe zidzawapeza; chisoni ndi kuusa moyo kudzachoka.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\c 36 \v 1 M'chaka cha 14 cha Mfumu Hezekiya, Senakeribu mfumu ya Asuri anaukira mizinda yonse ya Yuda yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri. \v 2 Pamenepo mfumu ya Asuri inatumiza kazembe wamkulu wa nkhondo kuchokera ku Lakisi kupita ku Yerusalemu kwa Mfumu Hezekiya ndi gulu lankhondo lalikulu. Adayandikira ngalande ya dziwe lakumtunda, panjira yayikulu yopita kumunda wa ochapa zovala, ndipo adayima pamenepo. \v 3 Aisraeli amene anatuluka mu mzindawo kukayankhula nawo anali Eliyakimu, mwana wa Hilikiya, woyang palaceanira nyumba yachifumu, Sebina mlembi wa mfumu, ndi Yowa mwana wa Asafu, amene analemba malamulo a boma.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 4 Mkulu wa asilikaliyo anawawuza kuti, "Uzani Hezekiya kuti mfumu yayikulu, mfumu ya Asuri, yanena kuti, 'Kodi ukudalira chiyani? \v 5 Mukungonena mawu opanda pake, kunena kuti pali uphungu ndi mphamvu zankhondo. wakhulupirira ndani wakupatsa iwe mphamvu kuti undiwukire?
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Mutu 36
|
|
@ -406,6 +406,10 @@
|
|||
"35-03",
|
||||
"35-05",
|
||||
"35-08",
|
||||
"35-10",
|
||||
"36-title",
|
||||
"36-01",
|
||||
"36-04",
|
||||
"38-title",
|
||||
"38-01",
|
||||
"38-04",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue