nya-x-nyanja_gen_text_reg/24/39.txt

1 line
391 B
Plaintext

\v 39 Nizamuuza bwana wanga, "nanga ngati mukazi sazanikonkha." \v 40 Koma ananiuza kuti, "Yehova wamene niyenda naye, azatuma mungelo na iwe nakukudalisa munjila yako, kuti umutengele mwana wanga kuchokela kuli ba bale banga na kuli ba banja ba batate. \v 41 Koma uzankhala omasuka ku chipangano changa ukabwela kuli ba bale banga iye kuli iwe. Ndipo uzankala omasuka ku chipangano changa.