nya-x-nyanja_gen_text_reg/06/09.txt

1 line
229 B
Plaintext

\v 9 Izi ndiye zamena zinacitika kwa Nowah. Nowah analiye munthu wolungama, ndipo pakati pa anthu analibe ili yonse pa nthuwi yake. \v 10 Nowa annayenda na Mulungu. Nowa anakhalatate wa bana bamuna batatu: Shemu, Hamu ndi Jafeti.