nya-x-nyanja_gen_text_reg/12/08.txt

1 line
257 B
Plaintext

\v 8 Kuchokela kuja ana vendela ku phiri yaku ziko yaku mawa mu Betele, kwamene anayika hema yake, na Betele kumazulo na Ai ku mawa. Kuja ana manga guwa ya Yehova nakuyitana pa zina la Yehova. \v 9 Ndipo Abramu anapitiliza ulendo, kuyenda moyagana ku Negev.