nya-x-nyanja_gen_text_reg/03/12.txt

1 line
251 B
Plaintext

\v 12 Mwamuna anakamba kuti, " Muzimai wamene munanipasa kunkhala naye, ananipasa cipaso camumtengo, ndipo ndinadya." \v 13 Yehova mulungu anakamba kuli mudzimai, " nivichani vamene wacita?" Muzimai anakamba kuti, " Njoka inani nama, ndipo ndinadya."