nya-x-nyanja_gen_text_reg/38/21.txt

1 line
422 B
Plaintext

\v 21 Waku adulamayiti anafunsa ba muna ba pa malo, "alikuti mukazi wachiwelwwele enze pa mbali pa njila ya Enami?" Banakamba kuti."kunalibe mukazi wachiwelwbwele pano." \v 22 Anabwele kuli Yuda anakamba kuti, "Sinamupeze. Nabamuna ba pamalo banakamba kuti, 'kuliba mukazi wechiwelewele pano." \v 23 Yuda anakamba kuti, mutekeni usunge vintu, kuti tisaletelewe nsoni, chifukwa, nonatuma ka mbuzi kang'ono koma sunamupeze."