nya-x-nyanja_gen_text_reg/38/12.txt

1 line
495 B
Plaintext

\v 12 Patapita ntawi itali, mwana mukazi wa Shua, mukazi wa Yuda, anafa. Yuda bana mutontoza ndipo anayenda kuli bo embela mbelele zake ku Tina , eve namukaze Hira waku Adulamayiti. \v 13 Tama bana muwuza, "wona, ba pongozi bako bamuna bayenda ku Tina kuyembela mbelele zake." \v 14 Anachosa zovala zamukazi wafedwa ndipo anazivwinikila na nyula nozimanga. anakhala pongenela mumalo ya Enami , inali pambali pa njila yaku Tina. chifukwa anawona kuti Sela akula koma sibanamukwatilise kuli eve.