nya-x-nyanja_gen_text_reg/49/05.txt

1 line
269 B
Plaintext

\v 5 Simeoni na Levi nipachi bululu. Vida va chongo ndiye mapanga yabo. \v 6 O moyo wanga, usangenemo muchiweruzo chabo; osangenemo mu musonkanonyao, pakuti mutima wanga uli na ulemu ngako pali icho. Pakuti mu ukali wao anapaya bantu, mukukondwela banalemalika ng'ombe.