nya-x-nyanja_gen_text_reg/46/33.txt

1 line
300 B
Plaintext

\v 33 Izafika ntawu pamene Farao azakwitanani no mifunsani kuti, nchito yanu nichani?' \v 34 Koma mukakambe, 'Banchito banu basunga nyama kuchokela ku bunyamata bwatu kufika manje, ise namakol atu. 'Chitani ivi chakuti munkale mu Malo ya Gosheni, osunga mbelele aliwonse niwonyasa kuli baku Igipito."