nya-x-nyanja_gen_text_reg/39/13.txt

1 line
315 B
Plaintext

\v 13 Ina bwela kuti, pamene anaona kuti psaya chovala mu manja naku tabila panja, \v 14 ana itana amuna ku nyumba naku bauza kuti, " Ona, Potifa ati letela muntu wachi Hebeli kuti sobelesa. Ezeli abwela kuti agone na ine ndipo napunda. \v 15 Zinaditika pamene napunda, ataba kusiya chovala naine, nakuyenda panja."