nya-x-nyanja_gen_text_reg/39/10.txt

1 line
296 B
Plaintext

\v 10 Anakamba na Yosefa siku na siku, koma anakana ku ngona nabo olo ku nkala naye. \v 11 Zina chitika kuti siku imozi anayenda ku sebenza ku nyumba. Amuna bonse sibana liko mu nyumba. \v 12 Anamu gwila pa chovela naku kamba, " Gona na ine." Anasiya chovala mu manje yake, kutaba, kuyenda panja.