nya-x-nyanja_gen_text_reg/21/17.txt

1 line
307 B
Plaintext

\v 17 Mulungu anamvela kulila kwa mwana, ndipo mungeli wa Mulungu anaitana kuli Haga ku chokela ku mwamba, naku kamba kuli eve, "Ni chani chaku vuta, Haga? Osa yopa chifukwa Mulungu anamvela kulila kwa mwana kwamene alili. \v 18 Nyamuka imika mwana nakumulibisa: chifukwa Nizampanga eve kunkhala ziko ikulu.