nya-x-nyanja_gen_text_reg/21/08.txt

1 line
201 B
Plaintext

\v 8 Mwana ana kula nakuleka ku nyonkha ndipo Abrahmu ana panda chikondwelelo chacikulu pamene ana siya ku nyoka Isaki. \v 9 Sara ana ona mwana wa Haga waku Egipito, wamene ana balila Abrahamu amuseka.