nya-x-nyanja_gen_text_reg/21/05.txt

1 line
314 B
Plaintext

\v 5 Abrahamu anali ana zaka handiladi pamene mwana wake Isaki anabandwa. \v 6 Sara anati, " Mulungu ani lengesa ku seka; bonse banza nvela baza seka naine." Ni ndani ana ganizila kuti. \v 7 Ndiposo Sara anati, " Ni ndani ana ganizila kuti Sara anga nkale na bana koma namu balila mwana mwamuna mubu nkalamba wake.