nya-x-nyanja_gen_text_reg/11/31.txt

1 line
305 B
Plaintext

\v 31 Tela ana tenga Abramu mwamuna wa mwana wake mwamuna Harani, na Sarai mupongozi wake, mukazi wamwana wake mwamuna abranu, ndipo pamozi bana choka mu Uri waku Kalidea, kuyenda ku Harani ya Kenani. Koma bana bwela ku Harani ndipo banankala kwamene. \v 32 Tela anankala zaka 205 ndipo anafela mu Harani.