nya-x-nyanja_gen_text_reg/11/27.txt

1 line
217 B
Plaintext

\v 27 Ndipo aba banli bana ba Tela. Tela anankala tate wa Abrahamu, Nahori, na Harani ndipo Horani anankala tate wa Loti. \v 28 Harani anafela pa pamenso ya Tela tate wake muziko yamene anabadwilamo ku Uri mu Kalidea.