nya-x-nyanja_gen_text_reg/05/12.txt

1 line
244 B
Plaintext

\v 12 Pamene Kenani anankhala zaka 70, anankhala tate wa Mahalaleli. \v 13 Pambuyo pake anankhala tate wa Mahalaleli, Kenani anankhala zaka 840. Anankhala tate wa bana bambili bamuna na bakazi. \v 14 Kenani anankhala zaka 910, ndipo anamwalila.