nya-x-nyanja_gen_text_reg/05/03.txt

1 line
277 B
Plaintext

\v 3 Pamene Adamu anankhala zaka 130, anankhala tate wamwana mwamuna olingana naye, namaonekedwe yake, anamupasa zina Seti. \v 4 Pamene Adamu anankhala tate wa Seti, anankhala zaka 800. Anankhala tate wa bana bambili bamuna na bakazi. \v 5 Adamu anankhala zaka 930 nakumwalila.