nya-x-nyanja_gen_text_reg/03/07.txt

1 line
295 B
Plaintext

\v 7 Menso yao wonse babili ya nasenguka, ndipo bana ziba kuti binali cinthuko. Anatenga matepo ya mutengo anampanga vovala vao. \v 8 Bana mvera mudidi ua Yehova Mulngu ayenda mu munda mumazulo, ndipo mwamuna na mukazi wake anazibisa beka kutoka ku menso ya Yehova mulungu mu mitengo zamu munda.