nya-x-nyanja_gen_text_reg/14/15.txt

1 line
248 B
Plaintext

\v 15 Iye ana gabanisa bantu bake bamuna usiku nakuyamba ku menyana nawo, naku bapisha m'paka ku Hoba, yamene ili ku m'polo kwa Damasikasi. \v 16 Ndipo anabwela na zafunikila zonse, na m'bululu wake Loti nazake gonse, na bazimayi na banthu benangu.